Baibulo
From Wikipedia, the free encyclopedia
Remove ads
Baibulo ndi buku lopatulika lomwe limakhulupiliwa kuti linapatsidwa kwa anthu kuchokera kwa Mulungu. Ilo lagawidwa muzigawo ziwiri- malemba a Chiheberi ndi malemba a Chigriki. Mabukhu amene amagwiritsidwa ntchito ku Chiyuda amatchedwa Tanaka kapena Baibulo la Chiyunda. Mabukhu amene amagwiritsidwa ntchito mu Chikhristu amatcheda Bukhu Loyera, Mau a Mulungu kapena Baibulo la chi Khristu. Chikhristu chimatenga ma bukhu ena a Baibulo la Chiyuda ku Chipangano cha kale, ngakhale ma bukhu awa amasiyana pa dongosolo lake ndipo ma baibulo ena ali ndi mabukhu owonjezera. baibulo la Chikhristu lili ndi mbali ina ya chiwiri yotchedwa Chipangano cha Tsopano.
- Buku Lopatulika ndilo Mau a Mulungu 1912 William Johnson.

Remove ads
Mabukhu a Baibulo
Ma bukhu a baibulo amayalidwa mofanana mu zitanthauziro zosiyana siyana. Baibulo la Chikhristu linagawidwa mbali ziwili: Chipangano cha Kale ndi Chipangano cha Tsopano.
Chipangano cha Kale
Genesis
Ekesodo
20
Numeri
Deuteronomo
Yoswa
Oweruza
Rute
1 Samueli
2 Samueli
1 Mafumu
2 Mafumu
1 Mbiri
2 Mbiri
Ezara
Nehemiya
Estere
Yobu
Masalimo
Miyambo
Mlaliki
Nyimbo ya Solomo
Yesaya
Yeremiya
Maliro
Ezekieli
Danieli
Hoseya
Yoweri
Obadiya
Yona
Mika
Nahamu
Habakuku
Zefaniya
Hagai
Zekariya
Malaki
Chipangano cha Tsopano
Mateyu
Maliko
Luka
Yohane
Machitidwe a Atumwi
Aroma
1 Akorinto
2 Akorinto
Afilipi
Akolose
1 Atesalonika
2 Atesalonika
1 Timoteyo
2 Timoteyo
Tito
Ahebri
Yakobo
1 Petro
2 Petro
1 Yohane
2 Yohane
3 Yohane
Yuda
Chibvumbulutso
Remove ads
Wikiwand - on
Seamless Wikipedia browsing. On steroids.
Remove ads
